Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 13:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndidzachititsa Amedi kuti awaukire,+

      Amene saona siliva ngati kanthu

      Ndipo sasangalala ndi golide.

      18 Mauta awo adzaphwanyaphwanya anyamata.+

      Iwo sadzamvera chisoni chipatso cha mimba

      Kapena kuchitira chifundo ana.

  • Danieli 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Zimene ndikufotokozere panopa ndi zoona:

      Mu ufumu wa Perisiya mudzakhala mafumu atatu amene adzalamulire, ndipo mfumu ya nambala 4 idzasonkhanitsa chuma chambiri kuposa ena onsewa. Ndipo ikadzangokhala yamphamvu chifukwa cha chuma chakecho, idzagwiritsa ntchito chilichonse pomenyana ndi ufumu wa Girisi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena