Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 102:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndithudi inu mudzanyamuka nʼkusonyeza Ziyoni chifundo,+

      Chifukwa imeneyi ndi nthawi yoti mumusonyeze kukoma mtima kwanu.+

      Nthawi yoikidwiratu yakwana.+

  • Yesaya 54:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 “Ndinakusiya kwa kanthawi kochepa,

      Koma ndidzakusonkhanitsa pamodzi mwachifundo chachikulu.+

       8 Chifukwa cha mkwiyo wanga waukulu ndinakubisira nkhope yanga kwa kanthawi,+

      Koma chifukwa cha chikondi changa chokhulupirika chimene sichidzatha ndidzakuchitira chifundo,”+ akutero Yehova, Wokuwombola.+

  • Yeremiya 14:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ngakhale kuti machimo athu akuchitira umboni kuti ndife olakwa,

      Inu Yehova, chitanipo kanthu chifukwa cha dzina lanu.+

      Chifukwa zochita zathu zosonyeza kusakhulupirika nʼzambiri,+

      Ndipo takuchimwirani.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena