Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ndiyeno magulu a asilikali ake* adzachitapo kanthu* ndipo adzaipitsa malo opatulika,+ malo okhala ndi mpanda wolimba kwambiri komanso adzachotsa nsembe zoyenera kuperekedwa nthawi zonse.+

      Iwo adzaika pamalowo chinthu chonyansa chobweretsa chiwonongeko.+

  • Maliko 13:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma mukadzaona chinthu chonyansa chobweretsa chiwonongeko+ chitaima pamalo amene sichikuyenera kuima (wowerenga adzazindikire), pamenepo amene ali mu Yudeya adzayambe kuthawira kumapiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena