Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 32:24-26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pomaliza, Yakobo anatsala yekhayekha. Kenako munthu winawake anayamba kulimbana naye mpaka mʼbandakucha.+ 25 Munthuyo ataona kuti Yakobo sakugonja, anamugwira pamalo amene fupa la ntchafu limalumikizana ndi chiuno ndipo polumikizanapo panaguluka mmene ankalimbana naye.+ 26 Atatero anauza Yakobo kuti: “Ndisiye ndizipita, chifukwa kukucha tsopano.” Koma Yakobo anayankha kuti: “Sindikusiya mpaka utandidalitsa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena