Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 17:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Aisiraeli ankachita zinthu zosayenera kwa Yehova Mulungu wawo. Anapitiriza kumanga malo okwezeka mʼmizinda yawo yonse,+ kuyambira kunsanja ya alonda mpaka kumzinda wokhala ndi mpanda wolimba kwambiri.* 10 Iwo anapitiriza kuika zipilala zopatulika ndi mizati yopatulika*+ paphiri lililonse lalitali ndi pansi pa mtengo uliwonse waukulu wa masamba obiriwira.+

  • Hoseya 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Efuraimu wapanga maguwa ansembe ambiri ndipo wachimwa.+

      Akugwiritsa ntchito maguwa akewa kuti azichimwa.+

  • Hoseya 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Isiraeli ndi mtengo wa mpesa wowonongeka* umene ukubereka zipatso.+

      Pamene zipatso zake zikuchuluka, mʼpamenenso akumanga maguwa ambiri.+

      Pamene zokolola zikuchuluka mʼdziko lake, mʼpamenenso akumanga zipilala zopatulika zokongola kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena