Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 33:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Iwe mwana wa munthu, lankhula ndi anthu a mtundu wako+ ndipo uwauze kuti,

      ‘Tiyerekeze kuti ndabweretsa lupanga mʼdziko,+ ndiyeno anthu onse amʼdzikolo asankha munthu kuti akhale mlonda wawo, 3 ndiye mlondayo waona lupanga likubwera kudzaukira dzikolo, nʼkuliza lipenga la nyanga ya nkhosa kuchenjeza anthu.+

  • Amosi 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Lipenga la nyanga ya nkhosa likalira mumzinda, kodi anthu sanjenjemera?

      Kodi tsoka likagwa mumzinda, si Yehova amene wachititsa?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena