Zefaniya 1:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Tsiku lalikulu la Yehova lili pafupi.+ Lili pafupi ndipo likubwera mofulumira kwambiri.+ Mkokomo wa tsiku la Yehova ukubwera ndi zowawa.+ Pa tsiku limenelo msilikali adzalira.+ Zefaniya 1:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Tsiku loliza lipenga ndiponso la mfuu yankhondo,+Pochenjeza mizinda ya mipanda yolimba komanso nsanja zazitali zamʼmakona.+ Malaki 4:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 “Taonani! Tsiku loyaka ngati ngʼanjo likubwera,+ ndipo anthu onse odzikuza ndi onse ochita zoipa adzakhala ngati mapesi. Pa tsikulo iwo adzawonongedwa moti sipadzatsala mizu kapena nthambi zawo,” watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.
14 Tsiku lalikulu la Yehova lili pafupi.+ Lili pafupi ndipo likubwera mofulumira kwambiri.+ Mkokomo wa tsiku la Yehova ukubwera ndi zowawa.+ Pa tsiku limenelo msilikali adzalira.+
16 Tsiku loliza lipenga ndiponso la mfuu yankhondo,+Pochenjeza mizinda ya mipanda yolimba komanso nsanja zazitali zamʼmakona.+
4 “Taonani! Tsiku loyaka ngati ngʼanjo likubwera,+ ndipo anthu onse odzikuza ndi onse ochita zoipa adzakhala ngati mapesi. Pa tsikulo iwo adzawonongedwa moti sipadzatsala mizu kapena nthambi zawo,” watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.