Yeremiya 30:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Mayo ine! Chifukwa tsiku limenelo lidzakhala lochititsa mantha.*+ Ndipo palibe lofanana nalo.Tsiku limenelo lidzakhala lamavuto kwa Yakobo. Koma adzapulumutsidwa mʼmavuto amenewa. Amosi 5:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 ‘Tsoka kwa anthu amene akulakalaka tsiku la Yehova!+ Kodi chidzakuchitikireni nʼchiyani pa tsiku la Yehova?+ Limeneli lidzakhala tsiku lamdima, osati kuwala.+ Zefaniya 1:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Tsiku limenelo ndi tsiku la mkwiyo,+Tsiku la masautso ndi zowawa,+Tsiku lowononga ndi la mphepo yamkuntho,Tsiku la mdima wochititsa mantha,+Tsiku la mitambo ndi la mdima wandiweyani,+
7 Mayo ine! Chifukwa tsiku limenelo lidzakhala lochititsa mantha.*+ Ndipo palibe lofanana nalo.Tsiku limenelo lidzakhala lamavuto kwa Yakobo. Koma adzapulumutsidwa mʼmavuto amenewa.
18 ‘Tsoka kwa anthu amene akulakalaka tsiku la Yehova!+ Kodi chidzakuchitikireni nʼchiyani pa tsiku la Yehova?+ Limeneli lidzakhala tsiku lamdima, osati kuwala.+
15 Tsiku limenelo ndi tsiku la mkwiyo,+Tsiku la masautso ndi zowawa,+Tsiku lowononga ndi la mphepo yamkuntho,Tsiku la mdima wochititsa mantha,+Tsiku la mitambo ndi la mdima wandiweyani,+