Yeremiya 4:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Yehova wanena kuti: “Ngati ungabwerere, iwe Isiraeli,Ngati ungabwerere kwa ineNdipo ngati ungachotse mafano ako onyansa pamaso panga,Sudzakhalanso moyo wothawathawa.+ Hoseya 12:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 “Choncho bwerera kwa Mulungu wako.+Uzisonyeza chikondi chokhulupirika ndi chilungamo,+Ndipo nthawi zonse uziyembekezera Mulungu wako. Hoseya 14:1, 2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 “Inu Aisiraeli, bwererani kwa Yehova Mulungu wanu,+Popeza mwapunthwa chifukwa cha zolakwa zanu. 2 Bwererani kwa Yehova ndi mawu amenewa.Uzani Mulungu kuti, ‘Tikhululukireni zolakwa zathu.+ Landirani zinthu zathu zabwino,Ndipo tidzakutamandani ndi pakamwa pathu+ ngati mmene tingaperekere nsembe kwa inu ana a ngʼombe amphongo.
4 Yehova wanena kuti: “Ngati ungabwerere, iwe Isiraeli,Ngati ungabwerere kwa ineNdipo ngati ungachotse mafano ako onyansa pamaso panga,Sudzakhalanso moyo wothawathawa.+
6 “Choncho bwerera kwa Mulungu wako.+Uzisonyeza chikondi chokhulupirika ndi chilungamo,+Ndipo nthawi zonse uziyembekezera Mulungu wako.
14 “Inu Aisiraeli, bwererani kwa Yehova Mulungu wanu,+Popeza mwapunthwa chifukwa cha zolakwa zanu. 2 Bwererani kwa Yehova ndi mawu amenewa.Uzani Mulungu kuti, ‘Tikhululukireni zolakwa zathu.+ Landirani zinthu zathu zabwino,Ndipo tidzakutamandani ndi pakamwa pathu+ ngati mmene tingaperekere nsembe kwa inu ana a ngʼombe amphongo.