Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:26, 27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndikanatha kunena kuti: “Ndidzawabalalitsa,

      Ndidzachititsa kuti anthu asakumbukirenso za iwo,”

      27 Koma ndinkaopa zimene mdani anganene,+

      Chifukwa adaniwo angaganize molakwika.+

      Iwo anganene kuti: “Tapambana chifukwa cha mphamvu zathu,+

      Si Yehova amene wachita zonsezi.”

  • Salimo 79:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Tithandizeni inu Mulungu amene mumatipulumutsa,+

      Chifukwa cha dzina lanu laulemerero.

      Tipulumutseni komanso mutikhululukire* machimo athu chifukwa cha dzina lanu.+

      10 Musalole kuti anthu a mitundu ina azinena kuti: “Mulungu wawo ali kuti?”+

      Anthu a mitundu ina adziwe ife tikuona

      Kuti mwabwezera magazi a atumiki anu amene anakhetsedwa.+

  • Mika 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mdani wanga adzaonanso zimenezi,

      Ndipo manyazi adzagwira amene ankandinena kuti:

      “Yehova Mulungu wako ali kuti?”+

      Maso anga adzamuyangʼana.

      Iye adzapondedwapondedwa ngati matope amumsewu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena