Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Hoseya 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ngakhale kuti inu Aisiraeli mukuchita chiwerewere,+

      Yuda asakhale ndi mlandu.+

      Musabwere ku Giligala+ kapena ku Beti-aveni,+

      Ndipo musalumbire kuti, ‘Mʼdzina la Yehova Mulungu wamoyo!’+

  • Amosi 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 ‘Bwerani ku Beteli anthu inu kuti mudzachite zolakwa,*+

      Bwerani ku Giligala kuti mudzawonjezere machimo.+

      Bweretsani nsembe zanu+ mʼmawa.

      Ndipo pa tsiku lachitatu, mubweretse chakhumi* chanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena