-
Yeremiya 51:58Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
58 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti:
“Ngakhale kuti mpanda wa Babulo ndi waukulu, wonse udzagwetsedwa,+
Ndipo ngakhale kuti mageti ake ndi ataliatali, adzawotchedwa.
Anthu adzagwira ntchito yotopetsa pachabe.
Mitundu ya anthu idzadzitopetsa ndi ntchito, koma ntchito yawoyo idzawonongedwa ndi moto.”+
-