Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 40:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mmisiri amapanga fano lachitsulo,*

      Mmisiri wina wa zitsulo amachikuta ndi golide,+

      Ndipo amachipangira matcheni asiliva.

  • Yesaya 46:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pali anthu amene amakhuthula golide mʼzikwama zawo.

      Amayeza siliva pasikelo.

      Iwo amalemba ganyu mmisiri wa zitsulo ndipo amapanga mulungu ndi zinthu zimenezi.+

      Kenako anthuwo amayamba kumuweramira ndi kumulambira.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena