Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 65:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Kumeneko sikudzakhalanso mwana wakhanda amene adzangokhala ndi moyo masiku ochepa okha,

      Kapena munthu wachikulire amene sadzakwanitsa zaka zimene munthu amafunika kukhala ndi moyo.

      Chifukwa aliyense amene adzamwalire ali ndi zaka 100 adzaonedwa ngati kamnyamata,

      Ndipo wochimwa adzatembereredwa, ngakhale atakhala ndi zaka 100.*

  • Yeremiya 30:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma iwe Yakobo mtumiki wanga usachite mantha,” akutero Yehova,

      “Ndipo iwe Isiraeli usaope.+

      Chifukwa ndidzakupulumutsa kuchokera kutali

      Ndidzapulumutsanso ana ako kuchokera kudziko limene anatengedwa kukakhala akapolo.+

      Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala mosatekeseka komanso mopanda zosokoneza.

      Sipadzakhala wowaopseza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena