Yeremiya 30:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Kwa iwo kudzamveka mawu oyamikira ndi phokoso la kuseka kwa anthu.+ Ndidzawachulukitsa moti sadzakhala ochepa.+Ndidzawachititsa kuti akhale ambiri,*Ndipo sadzakhala anthu ochepa.+ Yeremiya 31:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Choncho ndidzakumanganso ndipo udzakhalanso mtundu,+ Iwe namwali wa Isiraeli, udzanyamulanso maseche akoNʼkupita kukavina mosangalala.*+ Yeremiya 31:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 “Taonani! Masiku akubwera, pamene ndidzachititsa kuti nyumba ya Isiraeli ndi nyumba ya Yuda ikhalenso ndi anthu ochuluka komanso ziweto zambiri,” akutero Yehova.+ Zekariya 2:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Mngeloyo anauza mnzakeyo kuti: “Thamanga ukauze mnyamata uyo kuti, ‘“Mu Yerusalemu anthu azidzakhalamo+ ngati mzinda wopanda mpanda chifukwa cha anthu onse ndiponso ziweto zimene zili mmenemo.+
19 Kwa iwo kudzamveka mawu oyamikira ndi phokoso la kuseka kwa anthu.+ Ndidzawachulukitsa moti sadzakhala ochepa.+Ndidzawachititsa kuti akhale ambiri,*Ndipo sadzakhala anthu ochepa.+
4 Choncho ndidzakumanganso ndipo udzakhalanso mtundu,+ Iwe namwali wa Isiraeli, udzanyamulanso maseche akoNʼkupita kukavina mosangalala.*+
27 “Taonani! Masiku akubwera, pamene ndidzachititsa kuti nyumba ya Isiraeli ndi nyumba ya Yuda ikhalenso ndi anthu ochuluka komanso ziweto zambiri,” akutero Yehova.+
4 Mngeloyo anauza mnzakeyo kuti: “Thamanga ukauze mnyamata uyo kuti, ‘“Mu Yerusalemu anthu azidzakhalamo+ ngati mzinda wopanda mpanda chifukwa cha anthu onse ndiponso ziweto zimene zili mmenemo.+