Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 35:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anthu amene Yehova anawawombola adzabwerera+ ndipo adzafika ku Ziyoni akufuula mosangalala.+

      Chisangalalo chosatha chidzakhala ngati chisoti chachifumu kumutu kwawo.+

      Adzakhala okondwa ndi osangalala

      Ndipo chisoni ndi kubuula zidzachoka.+

  • Yesaya 61:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mʼmalo mwa manyazi, mudzalandira madalitso ochuluka kuwirikiza kawiri,

      Ndipo mʼmalo mochita manyazi, mudzafuula mosangalala chifukwa cha gawo lanu.

      Inde, mudzalandira madalitso owirikiza kawiri mʼdziko lanu,+

      Ndipo mudzasangalala mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena