Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 35:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anthu amene Yehova anawawombola adzabwerera+ ndipo adzafika ku Ziyoni akufuula mosangalala.+

      Chisangalalo chosatha chidzakhala ngati chisoti chachifumu kumutu kwawo.+

      Adzakhala okondwa ndi osangalala

      Ndipo chisoni ndi kubuula zidzachoka.+

  • Yeremiya 31:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwo adzabwera nʼkufuula mosangalala pamwamba pa phiri la Ziyoni.+

      Nkhope zawo zidzawala chifukwa cha ubwino wa* Yehova.

      Chifukwa cha mbewu, vinyo watsopano+ ndi mafuta,

      Ndiponso chifukwa cha ana a nkhosa ndi ana a ngʼombe.+

      Iwo adzakhala ngati dimba lothiriridwa bwino+

      Ndipo sadzakhalanso ofooka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena