Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Zekariya 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzateteza anthu ake.

      Adani awo adzawaponyera miyala ndi gulaye,* koma iwo adzawagonjetsa.+

      Iwo adzasangalala ndipo adzafuula ngati amwa vinyo.

      Adzakhala ngati mbale zolowa zodzaza vinyo,

      Ndiponso ngati magazi amene athiridwa mʼmakona a guwa lansembe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena