-
Malaki 1:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 “‘Mwana amalemekeza bambo ake+ ndipo wantchito amalemekeza mbuye wake. Ngati ine ndili bambo,+ ulemu wanga uli kuti?+ Ngati ndili ambuye,* nʼchifukwa chiyani simundiopa?’* ndikutero ine Yehova wa magulu ankhondo akumwamba kwa inu ansembe amene mukunyoza dzina langa.+
‘Koma inu mukunena kuti: “Kodi dzina lanu talinyoza bwanji?”’
-