Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Malaki 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “‘Mwana amalemekeza bambo ake+ ndipo wantchito amalemekeza mbuye wake. Ngati ine ndili bambo,+ ulemu wanga uli kuti?+ Ngati ndili ambuye,* nʼchifukwa chiyani simundiopa?’* ndikutero ine Yehova wa magulu ankhondo akumwamba kwa inu ansembe amene mukunyoza dzina langa.+

      ‘Koma inu mukunena kuti: “Kodi dzina lanu talinyoza bwanji?”’

  • 1 Akorinto 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma kwa ife Mulungu alipo mmodzi yekha,+ amene ndi Atate.+ Zinthu zonse zinachokera kwa iye, ndipo ifeyo ndife ake.+ Palinso Ambuye mmodzi, Yesu Khristu, amene zinthu zonse zinakhalapo kudzera mwa iye,+ ndipo ifeyo kudzera mwa iyeyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena