Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 21:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma iwo amauza Mulungu woona kuti, ‘Tisiyeni!

      Sitikufuna kudziwa njira zanu.+

      15 Kodi Wamphamvuyonse ndi ndani kuti timutumikire?+

      Ndipo kodi tingapindule chiyani ngati titamudziwa?’+

  • Salimo 73:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndithudi, ndayeretsa mtima wanga pachabe,

      Ndipo ndasamba mʼmanja mwanga pachabe posonyeza kuti ndine wosalakwa.+

      14 Ndinkavutika tsiku lonse,+

      Ndipo mʼmawa uliwonse ndinkadzudzulidwa.+

  • Yesaya 58:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 ‘Nʼchifukwa chiyani simukuona pamene tikusala kudya?+

      Ndipo nʼchifukwa chiyani simukuona tikamadzisautsa?’+

      Chifukwa chakuti pa tsiku lanu losala kudya mumachita zofuna zanu,*

      Ndipo mumapondereza antchito anu.+

  • Zefaniya 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa nthawi imeneyo ndidzafufuza ndi nyale mosamala kwambiri mu Yerusalemu,

      Ndipo ndidzaweruza anthu amene akukhala mosatekeseka* nʼkumaganiza kuti,

      ‘Yehova sadzachita zabwino kapena zoipa.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena