Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 61:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Wandituma kuti ndilengeze za chaka cha Yehova chokomera anthu mtima,*

      Ndi za tsiku lobwezera la Mulungu wathu,+

      Komanso kuti nditonthoze anthu onse amene akulira,+

       3 Kuti ndisamalire anthu onse amene akulirira Ziyoni,

      Kuti ndiwapatse nsalu yovala kumutu mʼmalo mwa phulusa,

      Kuti ndiwapatse mafuta kuti azisangalala mʼmalo molira,

      Kuti ndiwapatse chovala choti azivala ponditamanda mʼmalo mokhala otaya mtima.

      Ndipo iwo adzatchedwa mitengo ikuluikulu ya chilungamo,

      Yodzalidwa ndi Yehova kuti iyeyo alemekezedwe.*+

  • Mateyu 11:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Bwerani kwa ine inu nonse amene mukugwira ntchito yotopetsa ndi olemedwa ndipo ndidzakutsitsimulani.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena