Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 13:25-27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mwininyumba akadzanyamuka nʼkukiya chitseko, inu mudzaima panja nʼkumagogoda chitsekocho, ndipo mudzanena kuti, ‘Ambuye titsegulireni.’+ Koma iye adzakuyankhani kuti: ‘Sindikudziwa kumene mukuchokera.’ 26 Ndiyeno mudzayamba kunena kuti, ‘Tinkadya ndi kumwa pamaso panu ndipo inu munkaphunzitsa mʼmisewu yathu.’+ 27 Koma iye adzakuuzani kuti, ‘Sindikudziwa kumene mukuchokera. Chokani pamaso panga, inu nonse ochita zinthu zosalungama!’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena