Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 27:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Inu Yehova, Mulungu amene mumapereka moyo kwa anthu onse,* sankhani munthu woti azitsogolera gululi. 17 Musankhe munthu woti akhale mtsogoleri wawo pa zinthu zonse, woti aziwatsogolera pa zochita zawo zonse, kuti gulu la Yehova lisakhale ngati nkhosa zopanda mʼbusa.”

  • 1 Mafumu 22:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho Mikaya anati: “Ndikuona Aisiraeli onse atabalalika mʼmapiri+ ngati nkhosa zopanda mʼbusa. Ndipo Yehova anati: ‘Amenewa alibe mtsogoleri. Aliyense abwerere kunyumba kwake mwamtendere.’”

  • Ezekieli 34:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho zinamwazikana chifukwa zinalibe mʼbusa+ ndipo zinakhala chakudya cha zilombo zonse zakutchire.

  • Maliko 6:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Koma atatsika anaona gulu lalikulu la anthu ndipo anawamvera chisoni,+ chifukwa anali ngati nkhosa zimene zilibe mʼbusa.+ Ndiye anayamba kuwaphunzitsa zinthu zambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena