Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 4:30-32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Iye anapitiriza kuti: “Kodi Ufumu wa Mulungu tingauyerekeze ndi chiyani kapena tingaufotokoze ndi fanizo lotani? 31 Uli ngati kanjere ka mpiru,* kamene pa nthawi yofesa kamakhala kakangʼono kwambiri kuposa njere zonse zapadziko lapansi.+ 32 Koma akakafesa, kamamera nʼkukula kuposa mbewu zonse zakudimba ndipo kamapanga nthambi zikuluzikulu, moti mbalame zamumlengalenga zimatha kupeza malo okhala mumthunzi wake.”

  • Luka 13:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho anapitiriza kunena kuti: “Kodi Ufumu wa Mulungu uli ngati chiyani, nanga ndingauyerekezere ndi chiyani? 19 Uli ngati kanjere ka mpiru* kamene munthu anakatenga nʼkukadzala mʼmunda wake. Kenako kanamera nʼkukhala mtengo, moti mbalame zamumlengalenga zinamanga zisa munthambi zake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena