Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma ine ndikukuuzani kuti aliyense wopitiriza kupsera mtima+ mʼbale wake wapalamula mlandu wa kukhoti. Ndipo aliyense wonenera mʼbale wake mawu achipongwe wapalamula mlandu wa ku Khoti Lalikulu. Komanso aliyense wonena mnzake kuti, ‘Ndiwe chitsiru!’ adzapita ku Gehena* wamoto.+

  • Mateyu 5:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndiye ngati diso lako lakumanja limakuchimwitsa,* ulikolowole nʼkulitaya.+ Chifukwa ndi bwino kuti ukhale wopanda chiwalo chimodzi kusiyana ndi kuti thupi lako lonse lidzaponyedwe mʼGehena.*+

  • Maliko 9:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Ngati diso lako limakuchimwitsa,* ulitaye.+ Ndi bwino kuti ukalowe mu Ufumu wa Mulungu uli ndi diso limodzi, kusiyana nʼkuti uponyedwe mu Gehena* uli ndi maso onse awiri,+

  • Aroma 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa ngati mukukhala motsatira zofuna za thupi, ndiye kuti mosakayikira mudzafa.+ Koma mukalola kuti mphamvu ya mzimu ikuthandizeni kupha zochita za thupi, mudzakhala ndi moyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena