Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 10:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Tsopano anapitiriza ulendo wawo wopita ku Yerusalemu ndipo Yesu anali patsogolo pawo. Ophunzirawo anadabwa kwambiri ndipo anthu amene ankamutsatirawo anayamba kuchita mantha. Kachiwirinso anatengera pambali ophunzira 12 aja nʼkuyamba kuwauza zinthu izi zimene zinali zitatsala pangʼono kuti zimuchitikire:+

  • Luka 18:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Kenako anatengera pambali ophunzira 12 aja nʼkuwauza kuti: “Tamverani! Tsopano tikupita ku Yerusalemu ndipo zonse zimene zinalembedwa ndi aneneri zokhudza Mwana wa munthu zikakwaniritsidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena