Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 10:41-45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ophunzira 10 ena aja atamva zimenezi, anakwiya kwambiri ndi Yakobo komanso Yohane.+ 42 Koma Yesu anawaitana nʼkuwauza kuti: “Inu mukudziwa kuti amene amaoneka ngati* akulamulira anthu a mitundu ina, amapondereza anthu awo ndipo akuluakulu awo amasonyeza mphamvu zawo pa iwo.+ 43 Sizikuyenera kukhala choncho pakati panu. Koma aliyense amene akufuna kuti akhale wamkulu pakati panu akuyenera kukhala mtumiki wanu+ 44 ndipo amene akufuna kuti akhale woyamba pakati panu akuyenera kukhala kapolo wa onse. 45 Chifukwa ngakhale Mwana wa munthu sanabwere kudzatumikiridwa koma kudzatumikira+ ndi kudzapereka moyo wake dipo* kuti awombole anthu ambiri.”+

  • Luka 22:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kenako anayamba kukangana kwambiri za amene anali wamkulu kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena