Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 9:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 ndidzachotsa Aisiraeli mʼdziko limene ndawapatsa+ ndipo nyumba imene ndaiyeretsa chifukwa cha dzina langa, ndidzaichotsa pamaso panga.+ Aisiraeli adzatonzedwa ndi kunyozedwa pakati pa mitundu yonse ya anthu.+ 8 Nyumbayi idzakhala bwinja.+ Aliyense wodutsa pafupi adzayangʼana modabwa ndipo adzaimba mluzu nʼkunena kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani Yehova anachitira zimenezi dzikoli komanso nyumbayi?’+

  • Yeremiya 12:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 “Nyumba yanga ndaisiya.+ Ndasiya cholowa changa.+

      Wokondedwa wanga ndamupereka mʼmanja mwa adani ake.+

  • Yeremiya 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 ‘Koma mukapanda kumvera mawu amenewa, ndikulumbira pa dzina langa kuti nyumba iyi idzakhala bwinja,’ akutero Yehova.+

  • Mateyu 21:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Nʼchifukwa chake ndikukuuzani kuti, Ufumu wa Mulungu udzachotsedwa kwa inu nʼkuperekedwa ku mtundu wobereka zipatso zake.

  • Luka 21:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma mukadzaona magulu ankhondo atazungulira Yerusalemu,+ mudzadziwe kuti mzindawu watsala pangʼono kuwonongedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena