Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 19:24-26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Atatero anauza anthu amene anaima chapafupi kuti, ‘Mulandeni ndalama ya minayo nʼkuipereka kwa amene ali ndi ndalama za mina 10.’+ 25 Koma iwo anamuuza kuti, ‘Mbuyathu, iyetu ali ndi ndalama za mina 10!’— 26 ‘Ndithu ndikukuuzani, aliyense amene ali nazo, adzapatsidwa zinanso zambiri, koma amene alibe adzalandidwa ngakhalenso zimene ali nazo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena