Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Yudasi Isikariyoti, mmodzi wa ophunzira 12 aja, anachoka nʼkupita kwa ansembe aakulu kuti akapereke Yesu kwa iwo.+ 11 Atamva zimenezo, iwo anasangalala ndipo anamulonjeza kuti amupatsa ndalama zasiliva.+ Choncho iye anayamba kufunafuna mpata wabwino kuti amupereke.

  • Luka 22:3-6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Satana analowa mwa Yudasi, amene ankadziwika kuti Isikariyoti, mmodzi wa ophunzira 12 aja.+ 4 Iye anapita kukakambirana ndi ansembe aakulu ndi oyangʼanira kachisi za mmene angamuperekere kwa iwo.+ 5 Iwo anasangalala ndipo anagwirizana kuti amupatse ndalama zasiliva.+ 6 Choncho iye anavomereza, ndipo anayamba kufunafuna mpata wabwino kuti amupereke kwa iwo popanda gulu la anthu pafupi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena