Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Koma mmodzi mwa anthu amene anaimirira chapafupi anasolola lupanga lake nʼkutema nalo kapolo wa mkulu wa ansembe mpaka kuduliratu khutu lake.+

  • Luka 22:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Mmodzi wa iwo anatemadi kapolo wa mkulu wa ansembe nʼkuduliratu khutu lake lakumanja.+

  • Yohane 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Simoni Petulo, amene anali ndi lupanga, analisolola nʼkutema nalo kapolo wa mkulu wa ansembe mpaka kuduliratu khutu lake lakumanja.+ Kapoloyo dzina lake anali Makasi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena