Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 6:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ananena zimenezi chifukwa Herodeyo anatumiza anthu kuti akagwire Yohane nʼkumumanga ndipo anamutsekera mʼndende chifukwa cha Herodiya, mkazi wa mchimwene wake Filipo amene Herodeyo anakwatira.+ 18 Anachita zimenezi chifukwa Yohane ankauza Herode kuti: “Nʼzosaloleka kuti mutenge mkazi wa mchimwene wanu.”+

  • Luka 3:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno popeza kuti Yohane anadzudzula Herode wolamulira chigawo pa nkhani yokhudza Herodiya, mkazi wa mʼbale wake, komanso chifukwa cha zoipa zonse zimene Herode anachita, 20 Herode anawonjezera choipa china pa zonsezo: Anatsekera Yohane mʼndende.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena