Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 24:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Ngati mwamuna wakwatira mkazi koma mkaziyo sakumusangalatsa chifukwa wamupeza ndi vuto linalake, azimulembera kalata yothetsera ukwati+ nʼkumupatsa, ndipo azimuchotsa panyumba pake.+

  • Mateyu 5:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Pajanso anati: ‘Aliyense amene akuthetsa ukwati ndi mkazi wake, azipatsa mkaziyo kalata yothetsera ukwati.’+

  • Mateyu 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Iwo anamufunsa kuti: “Nanga nʼchifukwa chiyani Mose analamula kuti mwamuna azipereka kalata yothetsera ukwati kwa mkazi nʼkumusiya?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena