Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 3:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ine ndikukubatizani mʼmadzi chifukwa chakuti mwalapa,+ koma amene akubwera mʼmbuyo mwanga ndi wamphamvu kuposa ine, ndipo sindili woyenera kumuvula nsapato zake.*+ Ameneyo adzakubatizani ndi mzimu woyera+ komanso moto.+ 12 Fosholo yake youluzira mankhusu* ili mʼmanja mwake, ndipo malo ake opunthirapo mbewu adzawayeretseratu kuti mbee! Tirigu adzamututira munkhokwe, koma mankhusu adzawawotcha ndi moto+ umene sungazimitsidwe.”

  • Maliko 1:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Iye ankalalikira kuti: “Pambuyo pangapa pakubwera winawake wamphamvu kuposa ine amene sindili woyenera kuwerama nʼkumasula zingwe za nsapato zake.+ 8 Ine ndakubatizani ndi madzi, koma iye adzakubatizani ndi mzimu woyera.”+

  • Machitidwe 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano onse anali atasonkhana pamodzi pa tsiku la Chikondwerero cha Pentekosite.+

  • Machitidwe 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno onsewo anadzazidwa ndi mzimu woyera+ ndipo anayamba kulankhula zilankhulo zosiyanasiyana,* mogwirizana ndi mmene mzimuwo unawachititsira kulankhula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena