Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Samueli anatenga nyanga ya mafuta+ nʼkumudzoza azichimwene ake akuona. Kuyambira tsiku limenelo, mzimu wa Yehova unayamba kuthandiza Davide.+ Kenako Samueli anabwerera ku Rama.+

  • 1 Samueli 17:58
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 58 Ndiyeno Sauli anamufunsa kuti: “Mnyamata iwe, kodi bambo ako ndi ndani?” Davide anayankha kuti: “Ndine mwana wa mtumiki wanu Jese,+ wa ku Betelehemu.”+

  • Mateyu 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Jese anabereka Mfumu Davide.+

      Davide anabereka Solomo,+ yemwe mayi ake anali mkazi wa Uriya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena