Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 “Ndisanakuumbe mʼmimba, ndinkakudziwa,*+

      Ndipo usanabadwe,* ndinakusankha* kuti ugwire ntchito yopatulika.+

      Ndinakusankha kuti ukhale mneneri ku mitundu ya anthu.”

  • Aroma 9:10-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Lonjezolo silinaperekedwe pa nthawi iyi yokha. Linaperekedwanso pamene Rabeka ankayembekezera kubereka ana amapasa a Isaki kholo lathu lija.+ 11 Mapasawo asanabadwe ndiponso asanachite chabwino kapena choipa chilichonse, Mulungu anasonyeza kuti cholinga chake chidzadalira iye amene amaitana, osati zochita za munthu. 12 Choncho anauza Rabeka kuti: “Wamkulu adzakhala kapolo wa wamngʼono.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena