Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 22:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mukabwereketsa ndalama kwa munthu aliyense wosauka* pakati pa anthu anga, kwa munthu amene ali pafupi ndi inu, musakhale ngati munthu wopereka ngongole yakatapira kwa iye. Musamuuze kuti apereke chiwongoladzanja.+

  • Levitiko 25:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Mukamukongoza ndalama musamafunepo chiwongoladzanja+ kapena kumupatsa chakudya kuti mupezerepo phindu.

  • Deuteronomo 23:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mlendo mungamulipiritse chiwongoladzanja,+ koma mʼbale wanu musamamulipiritse chiwongoladzanja,+ kuti Yehova Mulungu wanu akudalitseni pa chilichonse chimene mukuchita mʼdziko limene mukupita kukalitenga kuti likhale lanu.+

  • Salimo 37:25, 26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndinali mwana ndipo tsopano ndakula,

      Koma sindinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa,+

      Kapena ana ake akupemphapempha chakudya.+

      26 Nthawi zonse amakongoza ena zinthu zake mokoma mtima,+

      Ndipo ana ake adzalandira madalitso.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena