Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 9:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ndiyeno Yesu anayamba ulendo woyendera mizinda ndi midzi yonse. Iye ankaphunzitsa mʼmasunagoge awo komanso kulalikira uthenga wabwino wa Ufumu ndipo ankachiritsa matenda amtundu uliwonse amene anthu ankadwala.+

  • Luka 4:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Koma iye anawauza kuti: “Ndikuyenera kukalengezanso uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu kumizinda ina, chifukwa ndi zimene Mulungu anandituma kudzachita.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena