Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 13:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma imene inafesedwa pamiyala, ndi munthu amene wamva mawu nʼkuwavomereza mwamsanga ndiponso mosangalala.+ 21 Komabe chifukwa chakuti amakhala alibe mizu amapitiriza kukula kwa nthawi yochepa. Koma akakumana ndi masautso kapena kuyamba kuzunzidwa chifukwa cha mawuwo, iye amapunthwa mwamsanga.

  • Maliko 4:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mofanana ndi zimenezi, mbewu zimene zafesedwa pamiyala ndi mawu amene afesedwa mwa anthu omwe amati akangomva mawuwo, amawalandira mosangalala.+ 17 Koma iwo amakhala opanda mizu ndipo amapitirizabe kwakanthawi. Ndiyeno akangoyamba kuvutitsidwa kapena kuzunzidwa chifukwa cha mawuwo, amapunthwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena