Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yesu ataona kuti gulu la anthu lamuzungulira, analamula kuti achoke nʼkupita kutsidya lina.+

  • Mateyu 8:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndiyeno atakwera mʼngalawa, ophunzira ake anamʼtsatira.+

  • Maliko 4:35, 36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Tsiku limenelo madzulo, iye anauza ophunzira ake kuti: “Tiyeni tiwolokere tsidya linalo.”+ 36 Choncho atauza gulu la anthulo kuti lizipita, ophunzirawo anachoka naye pangalawa imene anakwera ija, koma analinso ndi ngalawa zina.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena