Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 14:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pa nthawiyo Herode, wolamulira chigawo,* anamva za Yesu+ 2 ndipo anauza atumiki ake kuti: “Ameneyu ndi Yohane Mʼbatizi. Anauka kwa akufa ndiye nʼchifukwa chake akuchita ntchito zamphamvu.”+

  • Maliko 6:14-16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno Mfumu Herode inamva zimenezi chifukwa dzina la Yesu linatchuka kwambiri ndipo anthu ankanena kuti: “Yohane Mʼbatizi wauka kwa akufa nʼchifukwa chake akuchita ntchito zamphamvu.”+ 15 Koma ena ankanena kuti: “Ndi Eliya.” Ndipo ena ankanena kuti: “Ndi mneneri ngati mmene analili aneneri akale.”+ 16 Koma Herode atamva za Yesu ananena kuti: “Ndithu Yohane amene ndinamudula mutu uja waukitsidwadi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena