Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 17:14-16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atafika kufupi ndi gulu la anthu,+ mwamuna wina anamuyandikira ndipo anamugwadira nʼkunena kuti: 15 “Ambuye, muchitire chifundo mwana wanga wamwamuna, chifukwa akudwala matenda akugwa ndipo akuvutika kwambiri. Nthawi zambiri amagwera pamoto ndiponso mʼmadzi.+ 16 Ndinapita naye kwa ophunzira anu koma alephera kumuchiritsa.”

  • Maliko 9:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Munthu wina amene anali mʼgululo anamuyankha kuti: “Mphunzitsi, ine ndabweretsa mwana wanga wamwamuna kwa inu chifukwa ali ndi mzimu umene umamulepheretsa kulankhula.+ 18 Mzimuwo umati ukamugwira, umamugwetsera pansi. Akatero amachita thovu mʼkamwa komanso kukukuta mano ndipo amafooka. Ndinapempha ophunzira anu kuti autulutse koma alephera.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena