Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:34-36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Musaganize kuti ndinabwera kudzabweretsa mtendere padziko lapansi. Sindinabwere kuti ndidzabweretse mtendere koma lupanga.+ 35 Ndinabwera kudzagawanitsa anthu. Ndinabwera kudzachititsa kuti mwana wamwamuna atsutsane ndi bambo ake, mwana wamkazi atsutsane ndi mayi ake ndiponso kuti mkazi wokwatiwa atsutsane ndi apongozi ake aakazi.+ 36 Kunena zoona, adani a munthu adzakhala a mʼbanja lake lenileni.

  • Yohane 7:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ena ankanena kuti: “Khristu uja ndi ameneyu.”+ Koma ena ankati: “Kodi Khristu angachokere mu Galileya?+

  • Yohane 7:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Choncho gulu la anthulo linagawanika pa nkhani yokhudza iye.

  • Yohane 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno ena mwa Afarisiwo anayamba kunena kuti: “Munthu ameneyu si wochokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata.”+ Ena ankanena kuti: “Kodi munthu wochimwa angachite bwanji zizindikiro ngati zimenezi?”+ Choncho anthuwo anagawanika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena