Salimo 118:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Wodalitsidwa ndi amene akubwera mʼdzina la Yehova.+Tikupempha kuti Yehova akudalitseni mʼnyumba yake. Mateyu 21:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Komanso gulu la anthu limene linali patsogolo pake ndi mʼmbuyo mwake linkafuula kuti: “Mʼpulumutseni Mwana wa Davide!+ Wodalitsidwa ndi amene akubwera mʼdzina la Yehova!*+ Mʼpulumutseni kumwambamwambako!”+ Maliko 11:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndiyeno amene anali patsogolo komanso amene ankabwera mʼmbuyo ankafuula kuti: “Mʼpulumutseni!+ Wodalitsidwa ndi amene akubwera mʼdzina la Yehova!*+
26 Wodalitsidwa ndi amene akubwera mʼdzina la Yehova.+Tikupempha kuti Yehova akudalitseni mʼnyumba yake.
9 Komanso gulu la anthu limene linali patsogolo pake ndi mʼmbuyo mwake linkafuula kuti: “Mʼpulumutseni Mwana wa Davide!+ Wodalitsidwa ndi amene akubwera mʼdzina la Yehova!*+ Mʼpulumutseni kumwambamwambako!”+
9 Ndiyeno amene anali patsogolo komanso amene ankabwera mʼmbuyo ankafuula kuti: “Mʼpulumutseni!+ Wodalitsidwa ndi amene akubwera mʼdzina la Yehova!*+