Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako anagona pansi pa kamtengo kaja mpaka tulo tinamʼpeza. Mwadzidzidzi kunabwera mngelo ndipo anamukhudza+ nʼkumuuza kuti: “Dzuka udye.”+

  • 1 Mafumu 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Patapita kanthawi, mngelo wa Yehova uja anabweranso nʼkumukhudza ndipo anamuuza kuti: “Dzuka udye, popeza ulendowu ukhala wautali.”

  • Danieli 10:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno wooneka ngati munthu uja anandikhudzanso nʼkundipatsa mphamvu.+ 19 Kenako anandiuza kuti: “Iwe munthu wokondedwa kwambiri,*+ usachite mantha.+ Mtendere ukhale nawe.+ Limba mtima, ndithu limba mtima.” Akulankhula nane, ndinalimbikitsidwa ndipo ndinanena kuti: “Lankhulani mbuyanga chifukwa inu mwandilimbikitsa.”

  • Mateyu 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako Mdyerekezi uja anamusiya+ ndipo kunabwera angelo nʼkuyamba kumutumikira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena