Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pa nthawiyi, ansembe aakulu ndiponso akulu anasonkhana mʼbwalo lapanyumba ya mkulu wa ansembe dzina lake Kayafa.+

  • Luka 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mʼmasiku amenewo Anasi anali wansembe wamkulu ndipo Kayafa+ anali mkulu wa ansembe. Pa nthawiyo mawu a Mulungu anafika kwa Yohane+ mwana wa Zekariya mʼchipululu.+

  • Machitidwe 4:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Tsiku lotsatira, olamulira ndi akulu ndiponso alembi anasonkhana ku Yerusalemu. 6 Panalinso Anasi+ wansembe wamkulu, Kayafa,+ Yohane, Alekizanda ndiponso anthu onse omwe anali achibale a wansembe wamkuluyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena