Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 11:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mothandizidwa ndi mzimu wa Mulungu, mmodzi wa iwo dzina lake Agabo,+ analosera kuti padziko lonse lapansi+ padzagwa njala yaikulu. Izi zinachitikadi mʼnthawi ya Kalaudiyo.

  • Machitidwe 21:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma titakhala masiku ndithu, mneneri wina dzina lake Agabo+ anabwera kuchokera ku Yudeya. 11 Iye anafika kwa ife nʼkutenga lamba wa Paulo. Kenako anadzimanga mapazi ndi manja nʼkunena kuti: “Mzimu woyera wati, ‘Mwiniwake wa lambayu, Ayuda adzamumanga chonchi ku Yerusalemu+ nʼkumupereka kwa anthu a mitundu ina.’”+

  • 1 Timoteyo 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komabe mawu ouziridwa amanena momveka bwino kuti nthawi ina mʼtsogolo, chikhulupiriro cha anthu ena chidzatha chifukwa chomvetsera mawu ouziridwa omwe ndi osocheretsa,+ ndiponso zinthu zimene ziwanda zimaphunzitsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena