Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Zekariya 13:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 “Iwe lupanga, nyamuka ubaye mʼbusa wanga.+

      Ubaye munthu yemwe ndi mnzanga,” watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.

      “Ipha mʼbusa+ ndipo nkhosa zake zibalalike.+

      Ine ndidzalanga nkhosa zonyozeka.”

  • Mateyu 26:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Kenako Yesu anawauza kuti: “Nonsenu muthawa nʼkundisiya ndekha usiku uno, chifukwa Malemba amanena kuti: ‘Ndidzapha mʼbusa ndipo nkhosa zamʼgululo zidzabalalika.’+

  • Maliko 14:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Yesu anawauza kuti: “Nonsenu muthawa nʼkundisiya ndekha, chifukwa Malemba amanena kuti: ‘Ndidzapha mʼbusa+ ndipo nkhosa zidzabalalika.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena