Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 35:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Musamalandire dipo lowombolera moyo wa munthu amene wapha mnzake, chifukwa ndi woyenera kuphedwa. Aphedwe ndithu ameneyo.+

  • Luka 23:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma gulu lonse linafuula kuti: “Ameneyu muthane naye basi, koma ife mutimasulire Baraba!”+ 19 (Munthu ameneyu anaponyedwa mʼndende chifukwa cha kuukira boma kumene kunachitika mumzindawo komanso chifukwa chopha munthu.)

  • Machitidwe 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inde, inu munakana woyera ndi wolungamayo, ndipo munapempha kuti akumasulireni munthu wopha anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena