Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 27:55, 56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Komanso azimayi ambiri ochokera ku Galileya amene ankatsatira Yesu kuti azimutumikira, anali komweko nʼkumaonerera chapatali.+ 56 Ena mwa iwo anali Mariya wa ku Magadala, Mariya mayi a Yakobo ndi Yose, ndiponso panali mayi a Yakobo ndi Yohane.*+

  • Mateyu 27:61
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Koma Mariya wa ku Magadala ndi Mariya wina anatsalira komweko, atakhala pansi pafupi ndi mandawo.+

  • Maliko 15:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Panalinso azimayi amene ankaonerera chapatali ndithu. Ena mwa iwo anali Mariya wa ku Magadala, Mariya mayi a Yakobo Wamngʼono ndi Yose komanso panali Salome,+

  • Luka 23:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Anthu onse amene ankamudziwa anaimirira chapatali ndithu. Komanso azimayi amene anamutsatira kuchokera ku Galileya anali pomwepo ndipo anaona zinthu zimenezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena